Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 5:47 - Buku Lopatulika

47 Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Koma ngati simukhulupirira zimene iyeyo adalemba, nanga mungakhulupirire bwanji mau anga?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Koma ngati simukhulupirira zimene iye analemba, mudzakhulupirira bwanji zimene Ine ndikunena?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 5:47
3 Mawu Ofanana  

Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo.


Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.


ndi kuti kuyambira ukhanda wako wadziwa malembo opatulika, okhoza kukupatsa nzeru kufikira chipulumutso, mwa chikhulupiriro cha mwa Khristu Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa