Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:51 - Buku Lopatulika

51 Ndipo m'mene analikutsika, akapolo ake anakomana naye, nanena, kuti, Mwana wanu ali ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Ndipo m'mene analikutsika, akapolo ake anakomana naye, nanena, kuti, Mwana wanu ali ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Pa njira adakumana ndi antchito ake, ndipo iwo adamuuza kuti, “Mwana wanu wachira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Iye ali pa njira, antchito ake anakumana naye, namuwuza kuti mwana wanu uja wachira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:51
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya ananyamula mwanayo, natsika naye ku chipinda chosanja, nalowa naye m'nyumba, nampereka kwa amake; nati, Eliya, Taona, mwana wako ali moyo.


Yesu ananena naye, Muka, mwana wako ali ndi moyo. Munthuyo anakhulupirira mau amene Yesu anatero naye, namuka.


Chifukwa chake anawafunsa ora lake anayamba kuchiralo. Pamenepo anati kwa iye, kuti, Dzulo, ora lachisanu ndi chiwiri malungo anamsiya.


Chifukwa chake atateyo anadziwa kuti ndi ora lomwelo limene Yesu anati kwa iye, Mwana wako ali ndi moyo; ndipo anakhulupirira iye yekha ndi a pa banja lake onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa