Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:41 - Buku Lopatulika

41 Ndipo ambiri oposa anakhulupirira chifukwa cha mau ake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Ndipo ambiri oposa anakhulupirira chifukwa cha mau ake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Pamenepo anthu enanso ambiri adakhulupirira chifukwa cha mau a Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Ndipo chifukwa cha mawu ake, ena ambiri anakhulupirira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:41
13 Mawu Ofanana  

Ndodo yachifumu siidzachoka mwa Yuda, kapena wolamulira pakati pa mapazi ake, kufikira atadza Silo; ndipo anthu adzamvera iye.


chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro.


Chifukwa chake pamene Asamariya anadza kwa Iye, anamfunsa akhale nao; ndipo anakhala komweko masiku awiri.


ndipo ananena kwa mkazi, kuti, Tsopano sitikhulupirira chifukwa cha kulankhula kwako: pakuti tamva tokha, ndipo tidziwa kuti Mpulumutsi wa dziko lapansi ndi Iyeyu ndithu.


Wopatsa moyo ndi mzimu; thupi silithandiza konse. Mau amene ndalankhula ndi inu ndiwo mzimu, ndi moyo.


Anyamatawo anayankha, Nthawi yonse palibe munthu analankhula chotero.


Komatu mudzalandira mphamvu, Mzimu Woyera atadza pa inu: ndipo mudzakhala mboni zanga mu Yerusalemu, ndi mu Yudeya monse, ndi mu Samariya, ndi kufikira malekezero ake a dziko.


Ndipo iwo anaperekezedwa ndi Mpingo, napita pa Fenisiya ndi Samariya, nafotokozera chisanduliko cha amitundu; nakondweretsa kwambiri abale onse.


Koma pamene anakhulupirira Filipo wakulalikira Uthenga Wabwino wa Ufumu wa Mulungu ndi dzina la Yesu Khristu, anabatizidwa, amuna ndi akazi.


Pamenepo iwo, atatha kuchita umboni ndi kulankhula mau a Ambuye, anabwera kunka ku Yerusalemu, nalalikira Uthenga Wabwino kumidzi yambiri ya Asamariya.


Ndipo palibe cholembedwa chosaonekera pamaso pake, koma zonse zikhala za pambalambanda ndi zovundukuka pamaso pake pa Iye amene tichita naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa