Yohane 4:37 - Buku Lopatulika37 Pakuti m'menemo chonenacho chili choona, Wofesa ndi wina, womweta ndi winanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Pakuti m'menemo chonenacho chili choona, Wofesa ndi wina, womweta ndi winanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Paja amanenadi zoona aja amati, ‘Wobzala ndi wina, wokolola ndi winanso.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Nʼchifukwa chake mawu akuti, ‘Wina amafesa ndipo wina amakolola’ ndi woona. Onani mutuwo |