Yohane 4:29 - Buku Lopatulika29 Tiyeni, mukaone munthu, amene anandiuza zinthu zilizonse ndinazichita: ameneyu sali Khristu nanga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Tiyeni, mukaone munthu, amene anandiuza zinthu zilizonse ndinazichita: ameneyu sali Khristu nanga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 “Tiyeni, mukaone munthu amene wandiwuza zonse zimene ine ndidachita. Kodi ameneyu sangakhale Mpulumutsi wolonjezedwa uja kapena?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 “Tiyeni mukaone munthu amene wandiwuza ine zilizonse zimene ndinazichita. Kodi ameneyu sangakhale Khristu?” Onani mutuwo |