Yohane 4:13 - Buku Lopatulika13 Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso ludzu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso ludzu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Yesu adati, “Munthu aliyense womwako madzi aŵa, adzamvanso ludzu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu, Onani mutuwo |