Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:13 - Buku Lopatulika

13 Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso ludzu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso ludzu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Yesu adati, “Munthu aliyense womwako madzi aŵa, adzamvanso ludzu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:13
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anakweza mau nati, Atate Abrahamu, mundichitire chifundo, mutume Lazaro, kuti aviike nsonga ya chala chake m'madzi, naziziritse lilime langa; pakuti ndizunzidwadi m'lawi ili la moto.


Kodi muli wamkulu ndi atate wathu Yakobo amene anatipatsa ife chitsimechi, namwamo iye yekha, ndi ana ake, ndi zoweta zake?


koma iye wakumwa madzi amene Ine ndidzampatsa sadzamva ludzu nthawi zonse; koma madzi amene Ine ndidzampatsa adzakhala mwa iye kasupe wa madzi otumphukira kumoyo wosatha.


Gwirani ntchito si chifukwa cha chakudya chimene chitayika koma cha chakudya chimene chitsalira kumoyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani inu; pakuti ameneyo Atate, ndiye Mulungu, adamlembera chizindikiro.


Makolo anu adadya m'chipululu, ndipo adamwalira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa