Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 3:32 - Buku Lopatulika

32 Chimene anachiona nachimva, achita umboni wa ichi chomwe; ndipo kulibe munthu alandira umboni wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Chimene anachiona nachimva, achita umboni wa ichi chomwe; ndipo kulibe munthu alandira umboni wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Iyeyu akuchitira umboni zimene adaziwona ndi kuzimva komabe palibe amene amakhulupirira mau akewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Iye achita umboni pa zimene waziona ndi kuzimva, koma palibe avomereza umboni wake.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 3:32
13 Mawu Ofanana  

Chifukwa chanji ndinafika osapeza munthu? Ndi kuitana koma panalibe wina woyankha? Kodi dzanja langa lafupika konse, kuti silingathe kuombola? Pena Ine kodi ndilibe mphamvu zakupulumutsa? Taona pa kudzudzula kwanga ndiumitsa nyanja, ndi kusandutsa mitsinje chipululu; nsomba zake zinunkha chifukwa mulibe madzi, ndipo zifa ndi ludzu.


Ndani wamvera uthenga wathu? Ndi mkono wa Yehova wavumbulukira yani?


pakuti yense wakupempha alandira; ndi wakufunayo apeza; ndi kwa wogogodayo chitsegulidwa.


Anadza kwa zake za Iye yekha, ndipo ake a mwini yekha sanamlandire Iye.


Sinditchanso inu akapolo; chifukwa kapolo sadziwa chimene mbuye wake achita; koma ndatcha inu abwenzi; chifukwa zonse zimene ndazimva kwa Atate wanga ndakudziwitsani.


Pamenepo Pilato anati kwa Iye, Nanga kodi ndiwe Mfumu? Yesu anayankha, Munena kuti ndine Mfumu. Ndinabadwira ichi Ine, ndipo ndinadzera ichi kudza kudziko lapansi, kuti ndikachite umboni ndi choonadi. Yense wakukhala mwa choonadi amva mau anga.


Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Tilankhula chimene tichidziwa, ndipo tichita umboni za chimene tachiona; ndipo umboni wathu simuulandira.


Ndipo anadza kwa Yohane, nati kwa iye, Rabi, Iye amene anali ndi inu tsidya lija la Yordani, amene munamchitira umboni, taonani yemweyu abatiza, ndipo anthu onse alinkudza kwa Iye.


Iye amene analandira umboni wake anaikapo chizindikiro chake kuti Mulungu ali woona.


Pakuti Atate akonda Mwana, namuonetsa zonse azichita yekha: ndipo adzamuonetsa ntchito zoposa izi, kuti mukazizwe.


Ndili nazo zambiri zakulankhula ndi zakuweruza za inu; koma wondituma Ine ali woona; ndipo zimene ndazimva kwa Iye, zomwezo ndilankhula kwa dziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa