Yohane 3:33 - Buku Lopatulika33 Iye amene analandira umboni wake anaikapo chizindikiro chake kuti Mulungu ali woona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Iye amene analandira umboni wake anaikapo chizindikiro chake kuti Mulungu ali woona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma munthu akakhulupirira mau akeŵo, pamenepo amatsimikiza kuti Mulungu sanama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Munthu amene amawulandira akutsimikizira kuti Mulungu ndi woona. Onani mutuwo |