Yohane 3:20 - Buku Lopatulika20 Pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika, ndipo sakudza kwa kuunika, kuti zingatsutsidwe ntchito zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika, ndipo sakudza kwa kuunika, kuti zingatsutsidwe ntchito zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Aliyense wochita zoipa, amadana ndi kuŵala. Saonekera poyera, kuwopa kuti zochita zakezo zingaonekere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Aliyense wochita zoyipa amadana ndi kuwunika, ndipo sabwera poyera chifukwa cha mantha kuti ntchito zake zingaonekere. Onani mutuwo |