Yohane 3:15 - Buku Lopatulika15 kuti yense wakukhulupirira akhale nao moyo wosatha mwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 kuti yense wakukhulupirira akhale nao moyo wosatha mwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 kuti aliyense wokhulupirira akhale ndi moyo wosatha mwa Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. Onani mutuwo |
koma podziwa kuti munthu sayesedwa wolungama pa ntchito ya lamulo, koma mwa chikhulupiriro cha Yesu Khristu, ifedi tinakhulupirira kwa Khristu Yesu, kuti tikayesedwe olungama ndi chikhulupiriro cha Khristu, ndipo si ndi ntchito za lamulo; pakuti palibe munthu adzayesedwa wolungama ndi ntchito za lamulo.