Yohane 21:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo pamene anatulukira pamtunda, anapenya moto wamakala pomwepo, ndi kansomba kosanjikikako, ndi mkate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo pamene anatulukira pamtunda, anapenya moto wamakala pomwepo, ndi kansomba kosanjikikako, ndi mkate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pamene adafika pa mtunda, adaonapo moto wamakala, pali nsomba, ndiponso buledi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Atafika pa mtunda, iwo anaona moto wamakala pamenepo ndi nsomba, ndi buledi. Onani mutuwo |