Yohane 21:10 - Buku Lopatulika10 Yesu ananena nao, Tenganiko nsomba zimene mwazigwira tsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Yesu ananena nao, Tenganiko nsomba zimene mwazigwira tsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Yesu adaŵauza kuti, “Bwera nazoni nsomba zina zimene mwapha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Yesu anawawuza kuti, “Tabweretsa nsomba zina mwagwirazo.” Onani mutuwo |