Yohane 2:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Paska wa Ayuda unayandikira, ndipo Yesu anakwera kunka ku Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Paska wa Ayuda unayandikira, ndipo Yesu anakwera kunka ku Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Itayandikira nthaŵi ya Paska, chikondwerero cha Ayuda, Yesu adanyamuka kupita ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Nthawi ya Paska ya Ayuda itayandikira, Yesu anapita ku Yerusalemu. Onani mutuwo |