Yohane 19:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo Yesu anatuluka kunja, atavala korona waminga, ndi malaya achibakuwa. Ndipo ananena nao, Taonani munthuyu! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo Yesu anatuluka kunja, atavala korona waminga, ndi malaya achibakuwa. Ndipo ananena nao, Taonani munthuyu! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamene Yesu adatuluka, atavala nsangamutu ija ndi chovala chofiirira chija, Pilato adati, “Nayutu munthu uja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pamenepo Yesu anatuluka atavala nkhata yaminga ndi mkanjo wapepo ndipo Pilato anawawuza kuti, “Nayu munthu uja!” Onani mutuwo |