Yohane 19:41 - Buku Lopatulika41 Koma kunali munda kumalo kumene anapachikidwako, ndi m'mundamo munali manda atsopano m'mene sanaikidwemo munthu aliyense nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Koma kunali munda kumalo kumene anapachikidwako, ndi m'mundamo munali manda atsopano m'mene sanaikidwamo munthu aliyense nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Kumene Yesu adaapachikidwako kunali munda. Ndipo m'mundamo munali manda atsopano, amene anali asanaikemo munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Pamalo pamene anapachikidwa Yesu panali munda ndipo mʼmundamo munali manda atsopano mʼmene munali simunayikidwemo aliyense. Onani mutuwo |