Yohane 19:42 - Buku Lopatulika42 Pomwepo ndipo anaika Yesu, chifukwa cha tsiku lokonzera la Ayuda, pakuti mandawo anali pafupi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Pomwepo ndipo anaika Yesu, chifukwa cha tsiku lokonzera la Ayuda, pakuti mandawo anali pafupi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Tsono popeza kuti linali tsiku la Ayuda lokonzekera chikondwerero cha Paska, ndipo mandawo anali pafupi, adaika Yesu m'menemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Chifukwa linali Tsiku la Ayuda Lokonzekera ndi kuti mandawo anali pafupipo, iwo anayika Yesu mʼmenemo. Onani mutuwo |