Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 18:34 - Buku Lopatulika

34 Yesu anayankha, Kodi munena ichi mwa inu nokha, kapena ena anakuuzani za Ine?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Yesu anayankha, Kodi munena ichi mwa inu nokha, kapena ena anakuuzani za Ine?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Yesu adati, “Kodi mukunena zimenezi mwa inu nokha, kapena ena adakuuzani za Ine?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Yesu anafunsa kuti, “Kodi amenewo ndi maganizo anu wokha? Kapena kuti ena anakuwuzani za Ine?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:34
3 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake Pilato analowanso mu Pretorio, naitana Yesu, nati kwa Iye, Iwe ndiwe mfumu ya Ayuda kodi?


Pilato anayankha, Ndili ine Myuda kodi? Mtundu wako ndi ansembe aakulu anakupereka kwa ine; wachita chiyani?


Ndipo analowanso ku Pretorio, nanena kwa Yesu, Muchoka kuti? Koma Yesu sanamyankhe kanthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa