Yohane 18:35 - Buku Lopatulika35 Pilato anayankha, Ndili ine Myuda kodi? Mtundu wako ndi ansembe aakulu anakupereka kwa ine; wachita chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Pilato anayankha, Ndili ine Myuda kodi? Mtundu wako ndi ansembe aakulu anakupereka kwa ine; wachita chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Pilato adati, “Ine ndine Myuda kodi? Anthu a mtundu wako womwe ndiponso akulu a ansembe ndiwo akupereka kwa ine. Udachita chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Pilato anayankha kuti, “Kodi iwe ukuganiza kuti ine ndine Myuda? Ndi anthu ako ndi akulu a ansembe ako amene akupereka iwe kwa ine. Kodi walakwanji?” Onani mutuwo |