Yohane 18:23 - Buku Lopatulika23 Yesu anayankha iye, Ngati ndalankhula choipa, chita umboni wa choipacho, koma ngati bwino, undipandiranji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Yesu anayankha iye, Ngati ndalankhula choipa, chita umboni wa choipacho, koma ngati bwino, undipandiranji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Yesu adamuyankha kuti, “Ngati ndalankhula moipa, chitchule choipacho. Koma ngati ndalankhula moona, ukundimenyeranji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine ndanena kanthu kolakwika, chitirani umboni chimene ndalakwa. Koma ngati ndanena zoona, nʼchifukwa chiyani mwandimenya?” Onani mutuwo |