Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 18:24 - Buku Lopatulika

24 Koma Anasi adamtumiza Iye womangidwa kwa Kayafa mkulu wa ansembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Koma Anasi adamtumiza Iye womangidwa kwa Kayafa mkulu wa ansembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Anasi adatumiza Yesu ali chimangire kwa Kayafa, mkulu wa ansembe onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Kenaka Anasi anamutumiza Iye, ali womangidwabe, kwa Kayafa, mkulu wa ansembe.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:24
4 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo akugwira Yesu ananka naye kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene adasonkhana alembi ndi akulu omwe.


pa ukulu wansembe wao wa Anasi ndi Kayafa, panadza mau a Mulungu kwa Yohane mwana wa Zekariya m'chipululu.


nayamba kupita naye kwa Anasi; pakuti anali mpongozi wa Kayafa, amene anali mkulu wa ansembe chaka chomwecho.


Koma Simoni Petro ndi wophunzira wina anatsata Yesu. Koma wophunzira ameneyo anali wodziwika kwa mkulu wa ansembe, nalowa pamodzi ndi Yesu, m'bwalo la mkulu wa ansembe;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa