Yohane 17:10 - Buku Lopatulika10 chifukwa ali anu: ndipo zanga zonse zili zanu, ndi zanu zili zanga; ndipo ndilemekezedwa mwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 chifukwa ali anu: ndipo zanga zonse zili zanu, ndi zanu zili zanga; ndipo ndilemekezedwa mwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Zanga zonse nzanu, monga zanu zonse nzanga, motero ndimalemekezedwa mwa iwowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Zonse zimene Ine ndili nazo ndi zanu, ndipo zonse zimene Inu muli nazo ndi zanga. Choncho Ine ndalemekezedwa mwa iwowo. Onani mutuwo |