Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 16:6 - Buku Lopatulika

6 Koma chifukwa ndalankhula izi ndi inu chisoni chadzala mumtima mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Koma chifukwa ndalankhula izi ndi inu chisoni chadzala mumtima mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 M'mitima mwanu mwadzaza chisoni chifukwa ndakuuzani zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Muli ndi chisoni kwambiri chifukwa ndakuwuzani zimene.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 16:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene ananyamuka pakupemphera anadza kwa ophunzira, nawapeza ali m'tulo ndi chisoni,


Ndipo anati kwa iwo, Mau awa ndi otani mulandizanawo poyendayenda? Ndipo anaima ndi nkhope zao zachisoni.


Mtima wanu usavutike; mukhulupirira Mulungu, khulupirirani Inenso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa