Yohane 16:5 - Buku Lopatulika5 Koma tsopano ndimuka kwa Iye wondituma Ine; ndipo palibe wina mwa inu andifunsa Ine, Munka kuti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma tsopano ndimuka kwa Iye wondituma Ine; ndipo palibe wina mwa inu andifunsa Ine, Munka kuti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma tsopano ndikupita kwa amene adandituma, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe mwa inu wondifunsa kuti, ‘Mukupita kuti?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Tsopano Ine ndikupita kwa Iye amene anandituma koma palibe wina mwa inu akundifunsa kuti, ‘Kodi mukupita kuti?’ Onani mutuwo |