Yohane 15:18 - Buku Lopatulika18 Ngati dziko lapansi lida inu, mudziwa kuti lidada Ine lisanayambe kuda inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ngati dziko lapansi lida inu, mudziwa kuti lidada Ine lisanayambe kuda inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Ngati anthu odalira zapansipano adana nanu, kumbukirani kuti adadana ndi Ine asanadane nanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Ngati dziko lapansi lidana nanu, dziwani kuti linayamba kudana ndi Ine. Onani mutuwo |