Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 15:17 - Buku Lopatulika

17 Zinthu izi ndilamula inu, kuti mukondane wina ndi mnzake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Zinthu izi ndilamula inu, kuti mukondane wina ndi mnzake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Choncho lamulo langa ndi lakuti muzikondana.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Lamulo langa ndi ili: ‘Muzikondana.’

Onani mutuwo Koperani




Yohane 15:17
5 Mawu Ofanana  

Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake.


Lamulo langa ndi ili, kuti mukondane wina ndi mnzake, monga ndakonda inu.


Chitirani ulemu anthu onse. Kondani abale. Opani Mulungu, Chitirani mfumu ulemu.


Ndipo tsopano ndikupemphani, mkazi womveka inu, wosati monga kukulemberani lamulo latsopano, koma lomwelo tinali nalo kuyambira pachiyambi, kuti tikondane wina ndi mnzake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa