Yohane 15:12 - Buku Lopatulika12 Lamulo langa ndi ili, kuti mukondane wina ndi mnzake, monga ndakonda inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Lamulo langa ndi ili, kuti mukondane wina ndi mnzake, monga ndakonda inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Lamulo langa ndi lakuti muzikondana monga momwe Ine ndakukonderani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Lamulo langa ndi ili: ‘Kondanani wina ndi mnzake monga Ine ndakonda inu.’ Onani mutuwo |