Yohane 15:1 - Buku Lopatulika1 Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate wanga ndiye wam'munda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate wanga ndiye wam'munda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndi mlimi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndiye mwini munda. Onani mutuwo |