Yohane 14:1 - Buku Lopatulika1 Mtima wanu usavutike; mukhulupirira Mulungu, khulupirirani Inenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mtima wanu usavutike; mukhulupirira Mulungu, khulupirirani Inenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yesu adauza ophunzira akewo kuti “Mtima wanu usavutike. Khulupirirani Mulungu, khulupirirani Inenso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Mtima wanu usavutike. Khulupirirani Mulungu; khulupirirani Inenso. Onani mutuwo |