Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 13:38 - Buku Lopatulika

38 Yesu anayankha, Moyo wako kodi udzautaya chifukwa cha Ine? Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Asanalire tambala udzandikana Ine katatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Yesu anayankha, Moyo wako kodi udzautaya chifukwa cha Ine? Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Asanalire tambala udzandikana Ine katatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Apo Yesu adati, “Iweyo kutaya moyo wako chifukwa cha Ine! Ndithu ndikunenetsa kuti tambala asanalire, ukhala utandikana katatu kuti Ine sundidziŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Kenaka Yesu anayankha kuti, “Kodi iwe udzalolera kutaya moyo chifukwa cha Ine? Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti tambala asanalire, iwe udzandikana katatu!”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 13:38
16 Mawu Ofanana  

Kunyada kutsogolera kuonongeka; mtima wodzikuza ndi kutsogolera kuphunthwa.


Wokhulupirira mtima wakewake ali wopusa; koma woyenda mwanzeru adzapulumuka.


Kudzikuza kwa munthu kudzamchepetsa; koma wokhala ndi mtima wodzichepetsa adzalemekezedwa.


Yesu anati kwa iye, Indetu ndinena kwa iwe, kuti usiku uno, tambala asanalire, udzandikana Ine katatu.


Ndipo Yesu ananena naye, Ndithu ndinena ndi iwe, kuti lero, usiku uno, tambala asanalire kawiri, udzandikana Ine katatu.


Ndipo anati kwa Iye, Ambuye, ndilipo ndikapite ndi Inu kundende ndi kuimfa.


Ndipo Iye anati, Ndikuuza iwe, Petro, sadzalira tambala lero lino kufikira udzakana katatu kuti sundidziwa Ine.


Yesu anayankha iwo, Kodi mukhulupirira tsopano?


Ananena naye kachitatu, Simoni mwana wa Yona, kodi undikonda Ine? Petro anamva chisoni kuti anati kwa iye kachitatu, Kodi undikonda Ine? Ndipo anati kwa iye, Ambuye, mudziwa Inu zonse; muzindikira kuti ndikukondani Inu. Yesu ananena naye, Dyetsa nkhosa zanga.


Ndipo ichi chinachitika katatu; ndipo zinakwezekanso zonse kumwamba.


Chifukwa chake iye wakuyesa kuti ali chilili, ayang'anire kuti angagwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa