Yohane 13:3 - Buku Lopatulika3 Yesu, podziwa kuti Atate adampatsa Iye zonse m'manja mwake, ndi kuti anachokera kwa Mulungu, namuka kwa Mulungu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yesu, podziwa kuti Atate adampatsa Iye zonse m'manja mwake, ndi kuti anachokera kwa Mulungu, namuka kwa Mulungu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yesu ankadziŵa kuti Atate adapereka zinthu zonse m'manja mwake. Ankadziŵanso kuti adachokera kwa Mulungu, ndipo kuti akubwerera kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yesu podziwa kuti Atate anamupatsa Iye zonse mʼmanja mwake, ndi kuti Iye anachokera kwa Mulungu ndipo amabwerera kwa Mulunguyo; Onani mutuwo |