Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 13:25 - Buku Lopatulika

25 Iyeyu potsamira pomwepo, pa chifukwa cha Yesu, anena ndi Iye, Ambuye, ndiye yani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Iyeyu potsamira pomwepo, pa chifukwa cha Yesu, anena ndi Iye, Ambuye, ndiye yani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Pamenepo iyeyo adatsamira pachifukwa pa Yesu, namufunsa kuti, “Ambuye, mukunena yani kodi?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Atamutsamiranso Yesuyo, anamufunsa Iye kuti, “Ambuye, kodi ndani?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 13:25
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo mfumu Ahasuwero inalankhula, niti kwa mkazi wamkulu Estere, Ndani uyu, ali kuti iyeyu wadzazidwa mtima wake kuti azitero?


Pamenepo Simoni Petro anamkodola nanena naye, Utiuze ndiye yani amene anena za iye.


Petro, m'mene anacheuka, anapenya wophunzira amene Yesu anamkonda alikutsata, amenenso anatsamira pachifuwa pake pamgonero, nati, Ambuye, ndani iye wakupereka Inu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa