Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 13:24 - Buku Lopatulika

24 Pamenepo Simoni Petro anamkodola nanena naye, Utiuze ndiye yani amene anena za iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Pamenepo Simoni Petro anamkodola nanena naye, Utiuze ndiye yani amene anena za iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Tsono Simoni Petro adamkodola nati, “Taŵafunsa, kodi akunena yani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Simoni Petro anamukodola wophunzirayo ndi kuti, “Mufunseni akunena za yani.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 13:24
7 Mawu Ofanana  

Koma m'mene iye anatulukamo, sanathe kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya mu Kachisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.


ndipo anakodola anzao a m'ngalawa yinayo, adze awathangate. Ndipo anadza, nadzaza ngalawa zonse ziwiri, motero kuti zinalinkumira.


Koma mmodzi wa ophunzira ake, amene Yesu anamkonda, analikutsamira pa chifuwa cha Yesu.


Iyeyu potsamira pomwepo, pa chifukwa cha Yesu, anena ndi Iye, Ambuye, ndiye yani?


Koma m'mene adawatambasulira dzanja akhale chete, anawafotokozera umo adamtulutsira Ambuye m'ndende. Ndipo anati, Muwauze Yakobo ndi abale izi. Ndipo anatuluka napita kwina.


Ndipo Paulo ananyamuka, nakodola ndi dzanja, nati, Amuna a Israele, ndi inu akuopa Mulungu, mverani.


Ndipo m'mene adamlola, Paulo anaimirira pamakwerero, natambalitsira anthu dzanja; ndipo pokhala chete onse, analankhula nao m'chinenedwe cha Chihebri, nanena:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa