Yohane 13:22 - Buku Lopatulika22 Ophunzira analikupenyana wina kwa mnzake, ndi kusinkhasinkha kuti ananena za yani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ophunzira analikupenyana wina kwa mnzake, ndi kusinkhasinkha kuti ananena za yani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ophunzira aja adayamba kupenyetsetsana, osadziŵa konse kuti akunena yani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ophunzira ake anapenyetsetsana wina ndi mnzake, posadziwa kuti amanena za yani. Onani mutuwo |