Yohane 13:19 - Buku Lopatulika19 Kuyambira tsopano ndinena kwa inu, chisadachitike, kuti pamene chitachitika, mukakhulupirire kuti ndine amene. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Kuyambira tsopano ndinena kwa inu, chisadachitike, kuti pamene chitachitika, mukakhulupirire kuti ndine amene. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndikukuuziranitu zimenezi tsopano zisanachitike, kuti zikadzachitika, mudzakhulupirire kuti Ine ndinedi Ndilipo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “Ine ndikukuwuzani tsopano zisanachitike zimenezi, kuti pamene zachitika, mudzakhulupirire kuti Ine Ndine. Onani mutuwo |