Yohane 13:17 - Buku Lopatulika17 Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ngati mudziŵa zimenezi, ndinu odala mukamazichita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ngati inu mudziwa zinthu zimenezi, mudzakhala odala mukamazichita. Onani mutuwo |