Yohane 13:15 - Buku Lopatulika15 Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndakupatsani chitsanzo, kuti inunso muzichita monga momwe Ine ndakuchitirani inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ine ndakupatsani chitsanzo kuti muzichita monga Ine ndachitira. Onani mutuwo |