Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 13:15 - Buku Lopatulika

15 Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Ndakupatsani chitsanzo, kuti inunso muzichita monga momwe Ine ndakuchitirani inu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ine ndakupatsani chitsanzo kuti muzichita monga Ine ndachitira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 13:15
7 Mawu Ofanana  

Senzani goli langa, ndipo phunzirani kwa Ine; chifukwa ndili wofatsa ndi wodzichepetsa mtima: ndipo mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.


Ndipo Mulungu wa chipiriro ndi wa chitonthozo apatse inu kuti mukhale ndi mtima umodzi wina ndi mnzake, monga mwa Khristu Yesu;


ndipo yendani m'chikondi monganso Khristu anakukondani inu, nadzipereka yekha m'malo mwathu, chopereka ndi nsembe kwa Mulungu, ikhale fungo lonunkhira bwino.


Pakuti kudzachita ichi mwaitanidwa; pakutinso Khristu anamva zowawa m'malo mwanu, nakusiyirani chitsanzo kuti mukalondole mapazi ake;


osati monga ochita ufumu pa iwo a udindo wanu, koma okhala zitsanzo za gululo.


iye wakunena kuti akhala mwa Iye, ayeneranso mwini wake kuyenda monga anayenda Iyeyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa