Yohane 12:18 - Buku Lopatulika18 Chifukwa cha ichinso khamulo linadza kudzakomana ndi Iye, chifukwa anamva kuti Iye adachita chizindikiro ichi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Chifukwa cha ichinso khamulo linadza kudzakomana ndi Iye, chifukwa anamva kuti Iye adachita chizindikiro ichi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nchifukwa chake anthu onsewo adakamchingamira, popeza kuti anali atamva kuti Iye adaachita chizindikiro chozizwitsa chimenechi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Anthu ambiri, anapita kukakumana naye, chifukwa iwo anamva kuti Iye anachita chizindikiro chodabwitsachi. Onani mutuwo |