Yohane 12:19 - Buku Lopatulika19 Chifukwa chake Afarisi ananena wina ndi mnzake, Muona kuti simupindula kanthu konse; onani dziko litsata pambuyo pake pa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Chifukwa chake Afarisi ananena wina ndi mnzake, Muona kuti simupindula kanthu konse; onani dziko litsata pambuyo pake pa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pamenepo Afarisi adayamba kuuzana kuti, “Mukuwonatu kuti sitikuphulapo kanthu konse. Onani anthu onse akumthamangira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Choncho Afarisi anati kwa wina ndi mnzake, “Taonani, palibe chimene mwachitapo. Anthu onse akumutsatira Iye!” Onani mutuwo |