Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 12:14 - Buku Lopatulika

14 Koma Yesu, m'mene adapeza kabulu anakhala pamenepo; monga mulembedwa:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Koma Yesu, m'mene adapeza kabulu anakhala pamenepo; monga mulembedwa:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono Yesu adapeza mwanawabulu nakwerapo, monga akunenera Malembo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Yesu anapeza bulu wamngʼono ndi kukwerapo, monga kunalembedwa kuti:

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:14
6 Mawu Ofanana  

Kondwera kwambiri, mwana wamkazi wa Ziyoni; fuula mwana wamkazi wa Yerusalemu; taona, Mfumu yako ikudza kwa iwe; ndiye wolungama, ndi mwini chipulumutso; wofatsa ndi wokwera pabulu, ndi mwana wamphongo wa bulu.


anatenga makwata a kanjedza, natuluka kukakomana ndi Iye, nafuula, Hosana; wolemekezeka Iye wakudza m'dzina la Ambuye, ndiye mfumu ya Israele.


Usaope, mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako idza wokhala pa mwana wa bulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa