Yohane 12:15 - Buku Lopatulika15 Usaope, mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako idza wokhala pa mwana wa bulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Usaope, mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako idza wokhala pa mwana wa bulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Usaope, iwe mzinda wa Ziyoni. Ona, Mfumu yako ilikudza, yakwera pa mwanawabulu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Usachite mantha mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako ikubwera, itakhala pa mwana wabulu.” Onani mutuwo |