Yohane 11:26 - Buku Lopatulika26 ndipo yense wakukhala ndi moyo, nakhulupirira Ine, sadzamwalira nthawi yonse. Kodi ukhulupirira ichi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 ndipo yense wakukhala ndi moyo, nakhulupirira Ine, sadzamwalira nthawi yonse. Kodi ukhulupirira ichi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndipo aliyense amene ali ndi moyo nakhulupirira Ine, sadzafa konse. Kodi ukukhulupirira zimenezi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” Onani mutuwo |