Yohane 11:24 - Buku Lopatulika24 Marita ananena ndi Iye, Ndidziwa kuti adzauka m'kuuka tsiku lomaliza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Marita ananena ndi Iye, Ndidziwa kuti adzauka m'kuuka tsiku lomaliza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Marita adati, “Ndikudziŵa kuti adzauka podzauka anthu kwa akufa pa tsiku lomaliza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Marita anayankha kuti, “Ine ndikudziwa kuti adzauka pa kuukanso pa tsiku lomaliza.” Onani mutuwo |