Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:14 - Buku Lopatulika

14 Pamenepo Yesu anati kwa iwo momveka, Lazaro wamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Pamenepo Yesu anati kwa iwo momveka, Lazaro wamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono Yesu adaŵauza mosabisa kuti, “Lazaro wamwalira,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Ndipo kenaka anawawuza momveka kuti, “Lazaro wamwalira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:14
6 Mawu Ofanana  

Ndipo mauwo ananena poyera. Ndipo Petro anamtenga Iye, nayamba kumdzudzula.


Pamenepo Ayuda anamzungulira Iye, nanena ndi Iye, Kufikira liti musinkhitsasinkhitsa moyo wathu? Ngati Inu ndinu Khristu, tiuzeni momveka.


Koma Yesu adanena za imfa yake; koma iwowa anayesa kuti ananena za mpumulo wa tulo.


Ndipo ndikondwera chifukwa cha inu kuti kunalibe Ine komweko, chakuti mukakhulupirire; koma tiyeni, tipite kwa iye.


Zinthu izi ndalankhula ndi inu m'mafanizo; ikudza nthawi imene sindidzalankhula ndi inu m'mafanizo, koma ndidzakulalikirani inu m'mafanizo, koma ndidzakulalikirani inu momveka za Atate.


Ophunzira ake ananena, Onani, tsopano mulankhula zomveka, ndipo mulibe kunena chiphiphiritso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa