Yohane 11:14 - Buku Lopatulika14 Pamenepo Yesu anati kwa iwo momveka, Lazaro wamwalira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pamenepo Yesu anati kwa iwo momveka, Lazaro wamwalira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono Yesu adaŵauza mosabisa kuti, “Lazaro wamwalira, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo kenaka anawawuza momveka kuti, “Lazaro wamwalira. Onani mutuwo |