Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 10:42 - Buku Lopatulika

42 Ndipo ambiri anakhulupirira Iye komweko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ndipo ambiri anakhulupirira Iye komweko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Motero anthu ambiri adakhulupirira Yesu kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Ndipo pamalo amenewo ambiri anakhulupirira Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 10:42
7 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ambiri a mwa Ayuda amene anadza kwa Maria, m'mene anaona chimene anachita, anakhulupirira Iye.


Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge,


Koma pamene anali mu Yerusalemu pa Paska pachikondwerero, ambiri anakhulupirira dzina lake, pakuona zizindikiro zake zimene anachitazi.


Ndipo m'mzinda muja anthu Asamariya ambiri anamkhulupirira Iye chifukwa cha mau a mkazi, wochita umboniyo, kuti, Anandiuza ine zinthu zilizonse ndinazichita.


Ndipo ambiri oposa anakhulupirira chifukwa cha mau ake;


Koma ambiri a m'khamu la anthu anakhulupirira Iye; ndipo ananena, Pamene Khristu akadza kodi adzachita zizindikiro zambiri zoposa zimene adazichita ameneyo?


Pakulankhula Iye zimenezi ambiri anakhulupirira Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa