Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 10:39 - Buku Lopatulika

39 Anafunanso kumgwira Iye; ndipo anapulumuka m'dzanja lao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Anafunanso kumgwira Iye; ndipo anapulumuka m'dzanja lao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Pamenepo anthu aja adafunanso kumgwira, koma Iye adazemba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Iwo anafuna kumugwiranso koma anawapulumuka mʼmanja mwawo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 10:39
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga.


Ayuda anatolanso miyala kuti amponye Iye.


Pamenepo anafuna kumgwira Iye; koma palibe wina anamgwira kumanja, chifukwa nthawi yake siinafike.


Koma ena mwa iwo anafuna kumgwira Iye; koma palibe munthu anamgwira kumanja.


Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka mu Kachisi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa