Yohane 10:34 - Buku Lopatulika34 Yesu anayankha iwo, Kodi sikulembedwa m'chilamulo chanu, Ndinati Ine, Muli milungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Yesu anayankha iwo, Kodi sikulembedwa m'chilamulo chanu, Ndinati Ine, Muli milungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yesu adati, “Kodi m'Malamulo mwanu suja mudalembedwa kuti ‘Mulungu adati, Ndinu milungu?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Yesu anawayankha kuti, “Kodi sizinalembedwa mʼmalamulo anu kuti, ‘Ine ndanena kuti ndinu milungu?’ Onani mutuwo |