Yohane 10:35 - Buku Lopatulika35 Ngati anawatcha milungu iwo amene mau a Mulungu anawadzera (ndipo cholemba sichingathe kuthyoka), Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ngati anawatcha milungu iwo amene mau a Mulungu anawadzera (ndipo cholemba sichingathe kuthyoka), Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Paja mau a m'Malembo ngoona mpaka muyaya, ndipo Mwiniwakeyo adaŵatcha milungu anthu aja Iye ankalankhula nawoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Ngati anawatcha milungu anthu amene analandira mawu a Mulungu, pajatu Malemba sangasweke, Onani mutuwo |