Yohane 10:27 - Buku Lopatulika27 Nkhosa zanga zimva mau anga, ndipo Ine ndizizindikira, ndipo zinditsata Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Nkhosa zanga zimva mau anga, ndipo Ine ndizizindikira, ndipo zinditsata Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Nkhosa zanga zimamva mau anga. Ine ndimazidziŵa, ndipo zimanditsatira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nkhosa zanga zimamva mawu anga, Ine ndimazidziwa, ndipo zimanditsata Ine. Onani mutuwo |