Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 10:26 - Buku Lopatulika

26 Koma inu simukhulupirira, chifukwa simuli a mwa nkhosa zanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Koma inu simukhulupirira, chifukwa simuli a mwa nkhosa zanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Koma inu simukhulupirira konse, chifukwa simuli a m'gulu la nkhosa zanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 koma inu simukhulupirira chifukwa simuli a gulu lankhosa zanga.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 10:26
10 Mawu Ofanana  

Nkhosa zanga zimva mau anga, ndipo Ine ndizizindikira, ndipo zinditsata Ine.


Pamene adatulutsa zonse nkhosa zimtsata iye; chifukwa zidziwa mau ake.


Chinthu chonse chimene anandipatsa Ine Atate chidzadza kwa Ine; ndipo wakudza kwa Ine sindidzamtaya iye kunja.


Ndipo ananena, Chifukwa cha ichi ndinati kwa inu, kuti palibe munthu angathe kudza kwa Ine, koma ngati kupatsidwa kwa iye ndi Atate.


Iye wochokera kwa Mulungu amva zonena za Mulungu; inu simumva chifukwa chakuti simuli a kwa Mulungu.


Ife ndife ochokera mwa Mulungu; iye amene azindikira Mulungu atimvera; iye wosachokera mwa Mulungu satimvera ife. Momwemo tizindikira mzimu wa choonadi, ndi mzimu wa chisokeretso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa