Yohane 10:26 - Buku Lopatulika26 Koma inu simukhulupirira, chifukwa simuli a mwa nkhosa zanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma inu simukhulupirira, chifukwa simuli a mwa nkhosa zanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Koma inu simukhulupirira konse, chifukwa simuli a m'gulu la nkhosa zanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 koma inu simukhulupirira chifukwa simuli a gulu lankhosa zanga. Onani mutuwo |