Yohane 1:43 - Buku Lopatulika43 M'mawa mwake anafuna kutuluka kunka ku Galileya, napeza Filipo. Ndipo Yesu ananena naye, Tsata Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 M'mawa mwake anafuna kutuluka kunka ku Galileya, napeza Filipo. Ndipo Yesu ananena naye, Tsata Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 M'maŵa mwake Yesu adaganiza zopita ku Galileya. Adapeza Filipo, namuuza kuti, “Unditsate.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Pa tsiku lotsatira Yesu anaganiza zopita ku Galileya. Atamupeza Filipo, anati kwa iye, “Nditsate.” Onani mutuwo |